×

oh inu ana a Adamu! Musalole Satana kuti akunyengeni inu monga momwe 7:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:27) ayat 27 in Chichewa

7:27 Surah Al-A‘raf ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 27 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿يَٰبَنِيٓ ءَادَمَ لَا يَفۡتِنَنَّكُمُ ٱلشَّيۡطَٰنُ كَمَآ أَخۡرَجَ أَبَوَيۡكُم مِّنَ ٱلۡجَنَّةِ يَنزِعُ عَنۡهُمَا لِبَاسَهُمَا لِيُرِيَهُمَا سَوۡءَٰتِهِمَآۚ إِنَّهُۥ يَرَىٰكُمۡ هُوَ وَقَبِيلُهُۥ مِنۡ حَيۡثُ لَا تَرَوۡنَهُمۡۗ إِنَّا جَعَلۡنَا ٱلشَّيَٰطِينَ أَوۡلِيَآءَ لِلَّذِينَ لَا يُؤۡمِنُونَ ﴾
[الأعرَاف: 27]

oh inu ana a Adamu! Musalole Satana kuti akunyengeni inu monga momwe anawatulutsitsa makolo anu ku Paradiso, kuwavula nsalu zawo ndi kuwaonetsa maliseche awo. Ndithudi iye pamodzi ndi gulu lake, amakuonani inu kuchokera kumalo amene inu simungathe kuwaona. Ndithudi Ife tidawapanga a Satana kukhala othandiza anthu osakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يابني آدم لا يفتننكم الشيطان كما أخرج أبويكم من الجنة ينـزع عنهما, باللغة نيانجا

﴿يابني آدم لا يفتننكم الشيطان كما أخرج أبويكم من الجنة ينـزع عنهما﴾ [الأعرَاف: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu ana a Adam! Satana asakusokonezeni monga momwe adawatulutsira makolo anu m’Munda wamtendere ndi kuwavula onse awiri chovala chawo kuti awasonyeze umaliseche wawo. Ndithu iye ndi mtundu wake akukuonani pomwe inu simukuwaona. Ndithu asatana tawachita kukhala abwenzi a osakhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek