×

Mulungu adzati: “Lowani, mgulu la mitundu amene adalipo inu musanadze, anthu ndi 7:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:38) ayat 38 in Chichewa

7:38 Surah Al-A‘raf ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 38 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿قَالَ ٱدۡخُلُواْ فِيٓ أُمَمٖ قَدۡ خَلَتۡ مِن قَبۡلِكُم مِّنَ ٱلۡجِنِّ وَٱلۡإِنسِ فِي ٱلنَّارِۖ كُلَّمَا دَخَلَتۡ أُمَّةٞ لَّعَنَتۡ أُخۡتَهَاۖ حَتَّىٰٓ إِذَا ٱدَّارَكُواْ فِيهَا جَمِيعٗا قَالَتۡ أُخۡرَىٰهُمۡ لِأُولَىٰهُمۡ رَبَّنَا هَٰٓؤُلَآءِ أَضَلُّونَا فَـَٔاتِهِمۡ عَذَابٗا ضِعۡفٗا مِّنَ ٱلنَّارِۖ قَالَ لِكُلّٖ ضِعۡفٞ وَلَٰكِن لَّا تَعۡلَمُونَ ﴾
[الأعرَاف: 38]

Mulungu adzati: “Lowani, mgulu la mitundu amene adalipo inu musanadze, anthu ndi majin, kupita ku moto, ndipo pamene uzidzalowa mtundu uliwonse udzakhala uli kutemberera mtundu umene udalipo iwo usanadze mpaka pamene adzasonkhanitsidwa onse m’moto ndipo mtundu womaliza udzati kwa mtundu woyambirira, ‘Ambuye wathu! Awa ndiwo anthu amene adatisokoneza ife motero apatseni chilango choonjezedwa kawiri m’moto.” Iye adzati: “Kwa aliyense kuli chilango chowilikiza koma inu simudziwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال ادخلوا في أمم قد خلت من قبلكم من الجن والإنس في, باللغة نيانجا

﴿قال ادخلوا في أمم قد خلت من قبلكم من الجن والإنس في﴾ [الأعرَاف: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“(Allah) adzati (pa tsiku la chiweruziro): “Lowani ku Moto pamodzi ndi mibadwo imene idamuka kale (inu musanabwere) yochokera m’ziwanda ndi mu anthu. M’badwo uliwonse pamene uzikalowa, udzatembelera unzake, kufikira pamene onse adzasonkhana m’menemo. Adzanena apambuyo kwa oyambilira awo: “Mbuye wathu! Awa, adatisokeretsa. Apatseni chilango cha Moto chochuluka.” (Allah) adzanena: “Aliyense mwa inu akhala ndi chilango chochuluka; koma izi inu simukudziwa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek