×

Ndipo anthu okhala ku Paradiso adzaitana anthu a ku Moto. “Ndithudi chimene 7:44 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:44) ayat 44 in Chichewa

7:44 Surah Al-A‘raf ayat 44 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 44 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَنَادَىٰٓ أَصۡحَٰبُ ٱلۡجَنَّةِ أَصۡحَٰبَ ٱلنَّارِ أَن قَدۡ وَجَدۡنَا مَا وَعَدَنَا رَبُّنَا حَقّٗا فَهَلۡ وَجَدتُّم مَّا وَعَدَ رَبُّكُمۡ حَقّٗاۖ قَالُواْ نَعَمۡۚ فَأَذَّنَ مُؤَذِّنُۢ بَيۡنَهُمۡ أَن لَّعۡنَةُ ٱللَّهِ عَلَى ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[الأعرَاف: 44]

Ndipo anthu okhala ku Paradiso adzaitana anthu a ku Moto. “Ndithudi chimene adatilonjeza ife Ambuye wathu tachipeza kuti ndi choona. Kodi inu mwapeza chomwe adakulonjezani Ambuye wanu kuti ndi choona?” Iwo adzati: Inde. Ndipo wofuula adzanena pakati pawo: “Matemberero a Mulungu ali pa anthu olakwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ونادى أصحاب الجنة أصحاب النار أن قد وجدنا ما وعدنا ربنا حقا, باللغة نيانجا

﴿ونادى أصحاب الجنة أصحاب النار أن قد وجدنا ما وعدنا ربنا حقا﴾ [الأعرَاف: 44]

Khaled Ibrahim Betala
“Anthu a ku Munda wamtendere adzaitana anthu aku Moto (adzanena kuti): “Ndithudi ife tapeza zimene Mbuye wathu adatilonjeza kuti nzoona. Kodi nanunso mwapeza zomwe Mbuye wanu adakulonjezani kuti nzoona?” (Anthu a ku Moto) adzanena: “Inde.” Choncho wolengeza pakati pawo adzalengeza kuti: “Matembelero a Allah ali pa anthu ochita zoipa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek