×

Ndipo Ife tidzachotsa chidani m’mitima mwawo ndipo mitsinje idzayenda pansi pa mapazi 7:43 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:43) ayat 43 in Chichewa

7:43 Surah Al-A‘raf ayat 43 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 43 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَنَزَعۡنَا مَا فِي صُدُورِهِم مِّنۡ غِلّٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهِمُ ٱلۡأَنۡهَٰرُۖ وَقَالُواْ ٱلۡحَمۡدُ لِلَّهِ ٱلَّذِي هَدَىٰنَا لِهَٰذَا وَمَا كُنَّا لِنَهۡتَدِيَ لَوۡلَآ أَنۡ هَدَىٰنَا ٱللَّهُۖ لَقَدۡ جَآءَتۡ رُسُلُ رَبِّنَا بِٱلۡحَقِّۖ وَنُودُوٓاْ أَن تِلۡكُمُ ٱلۡجَنَّةُ أُورِثۡتُمُوهَا بِمَا كُنتُمۡ تَعۡمَلُونَ ﴾
[الأعرَاف: 43]

Ndipo Ife tidzachotsa chidani m’mitima mwawo ndipo mitsinje idzayenda pansi pa mapazi awo ndipo iwo adzati: “Kuyamikidwa ndi kwa Mulungu amene watitsogolera ife ku izi ndipo ife sitikadakhala otsogozedwa pakadapanda Mulungu kutitsogolera! Ndithudi Atumwi a Ambuye wathu adadza ndi choonadi.” Ndipo zidzanenedwa kwa iwo kuti: “Iyi ndiyo Paradiso imene mwailandira chifukwa cha ntchito zanu zimene mudali kuchita.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ونـزعنا ما في صدورهم من غل تجري من تحتهم الأنهار وقالوا الحمد, باللغة نيانجا

﴿ونـزعنا ما في صدورهم من غل تجري من تحتهم الأنهار وقالوا الحمد﴾ [الأعرَاف: 43]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tidzachotsa kusakondana (komwe kudali) m’mitima mwawo; (adzakhala okondana ngakhale pa dziko lapansi adali odana), uku pansi ndi patsogolo pawo mitsinje ikuyenda; ndipo adzanena (m’kuthokoza kwawo): “Kuyamikidwa konse nkwa Allah, Yemwe adatitsogolera ku ichi (chomwe chatidzetsera mtendere). Sitikadaongoka pakadapanda Allah kutiongola. Atumiki a Mbuye wathu adadza ndi choonadi.” Ndipo adzaitanidwa (ndi kuuzidwa kuti): “Uwu ndi Munda wamtendere umene mwapatsidwa chifukwa cha zomwe mudali kuchita.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek