×

Nowa adati: “oh Ambuye! Anthu anga sali kundimvera ine koma mmalo mwake 71:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Nuh ⮕ (71:21) ayat 21 in Chichewa

71:21 Surah Nuh ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Nuh ayat 21 - نُوح - Page - Juz 29

﴿قَالَ نُوحٞ رَّبِّ إِنَّهُمۡ عَصَوۡنِي وَٱتَّبَعُواْ مَن لَّمۡ يَزِدۡهُ مَالُهُۥ وَوَلَدُهُۥٓ إِلَّا خَسَارٗا ﴾
[نُوح: 21]

Nowa adati: “oh Ambuye! Anthu anga sali kundimvera ine koma mmalo mwake ali kutsatira amene sangawaonjezere chuma ndi ana koma mavuto.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال نوح رب إنهم عصوني واتبعوا من لم يزده ماله وولده إلا, باللغة نيانجا

﴿قال نوح رب إنهم عصوني واتبعوا من لم يزده ماله وولده إلا﴾ [نُوح: 21]

Khaled Ibrahim Betala
“Adanena Nuh: “Mbuye wanga! Ndithu anthu anga andinyoza (pa zimene ndawalamula kuti akhulupirire Inu ndi kupempha chikhululuko chanu), ndipo (ofooka mwa iwo) amtsatira yemwe chuma chake ndi ana ake sizidzamuonjezera (chilichonse chabwino) koma kutaika (ndi kuonongeka pa tsiku lachimaliziro)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek