×

‘Ife sitidziwa ngati akuwafunira mavuto anthu awo amene ali padziko lapansi kapena 72:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jinn ⮕ (72:10) ayat 10 in Chichewa

72:10 Surah Al-Jinn ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jinn ayat 10 - الجِن - Page - Juz 29

﴿وَأَنَّا لَا نَدۡرِيٓ أَشَرٌّ أُرِيدَ بِمَن فِي ٱلۡأَرۡضِ أَمۡ أَرَادَ بِهِمۡ رَبُّهُمۡ رَشَدٗا ﴾
[الجِن: 10]

‘Ife sitidziwa ngati akuwafunira mavuto anthu awo amene ali padziko lapansi kapena kuti Ambuye wawo ali ndi cholinga choti awatsogolere

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأنا لا ندري أشر أريد بمن في الأرض أم أراد بهم ربهم, باللغة نيانجا

﴿وأنا لا ندري أشر أريد بمن في الأرض أم أراد بهم ربهم﴾ [الجِن: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu ife sitikudziwa chilango chimene akuwafunira a m’dziko (polondera kumwamba, kuletsa kumvetsera nkhani zakumeneko); kapena Mbuye wawo akuwafunira zabwino ndi chilungamo (pa zimenezo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek