×

Ndipo adzazunguliridwa ndi ana owatumikira a misinkhu yofanana. Ndipo ngati iwe utawaona 76:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Insan ⮕ (76:19) ayat 19 in Chichewa

76:19 Surah Al-Insan ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Insan ayat 19 - الإنسَان - Page - Juz 29

﴿۞ وَيَطُوفُ عَلَيۡهِمۡ وِلۡدَٰنٞ مُّخَلَّدُونَ إِذَا رَأَيۡتَهُمۡ حَسِبۡتَهُمۡ لُؤۡلُؤٗا مَّنثُورٗا ﴾
[الإنسَان: 19]

Ndipo adzazunguliridwa ndi ana owatumikira a misinkhu yofanana. Ndipo ngati iwe utawaona ukhoza kuganiza kuti ndi ndolo zomwazikamwazika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويطوف عليهم ولدان مخلدون إذا رأيتهم حسبتهم لؤلؤا منثورا, باللغة نيانجا

﴿ويطوف عليهم ولدان مخلدون إذا رأيتهم حسبتهم لؤلؤا منثورا﴾ [الإنسَان: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo azikawazungulira anyamata osasinthika (chilengedwe chawo,) utawaona (chifukwa cha kukongola kwawo ndi kuwala kwa nkhope zawo) ungawaganizire kuti ndi ngale zomwazidwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek