×

Ngakhale Mulungu akadadziwa ubwino umene uli mwa iwo, ndithudi, Iye akadawapanga kumva 8:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:23) ayat 23 in Chichewa

8:23 Surah Al-Anfal ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 23 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿وَلَوۡ عَلِمَ ٱللَّهُ فِيهِمۡ خَيۡرٗا لَّأَسۡمَعَهُمۡۖ وَلَوۡ أَسۡمَعَهُمۡ لَتَوَلَّواْ وَّهُم مُّعۡرِضُونَ ﴾
[الأنفَال: 23]

Ngakhale Mulungu akadadziwa ubwino umene uli mwa iwo, ndithudi, Iye akadawapanga kumva koma ngakhale Iye akadawapanga kuti azimva, iwo akadabwerera m’mbuyo ndi kukana choonadi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو علم الله فيهم خيرا لأسمعهم ولو أسمعهم لتولوا وهم معرضون, باللغة نيانجا

﴿ولو علم الله فيهم خيرا لأسمعهم ولو أسمعهم لتولوا وهم معرضون﴾ [الأنفَال: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah akadadziwa mwa iwo (ndi kudziwa kwake kopanda chiyambi); kuti muli ubwino (pakuwamveretsa Qur’an ndi kuwazindikiritsa) akadawamveretsa. (Koma chikhalidwe chawo chili cha mtundu umenewo) ndipo ngakhale akadawamveretsa (Qur’an ndikuwazindikiritsa) akadatembenuka m’mbuyo uku akunyoza (chifukwa cha kugonjera zilakolako zawo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek