×

oh inu anthu okhulupirira! Musamunyenge Mulungu ndi Mtumwi ndipo musachite chinyengo pamene 8:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:27) ayat 27 in Chichewa

8:27 Surah Al-Anfal ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 27 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَا تَخُونُواْ ٱللَّهَ وَٱلرَّسُولَ وَتَخُونُوٓاْ أَمَٰنَٰتِكُمۡ وَأَنتُمۡ تَعۡلَمُونَ ﴾
[الأنفَال: 27]

oh inu anthu okhulupirira! Musamunyenge Mulungu ndi Mtumwi ndipo musachite chinyengo pamene muli nkudziwa pophwanya malonjezo anu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا لا تخونوا الله والرسول وتخونوا أماناتكم وأنتم تعلمون, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا لا تخونوا الله والرسول وتخونوا أماناتكم وأنتم تعلمون﴾ [الأنفَال: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Musachitire Allah ndi Mtumiki (Wake) chinyengo (pa kutsata zimene mwaletsedwa). Ndipo musazichitire chinyengo zimene mwakhulupirika nazo uku mukudziwa (kuti kutero ndikulakwa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek