×

Amenyeni kuti Mulungu awalange iwo ndi manja anu ndi kuwachititsa manyazi, ndi 9:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:14) ayat 14 in Chichewa

9:14 Surah At-Taubah ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 14 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿قَٰتِلُوهُمۡ يُعَذِّبۡهُمُ ٱللَّهُ بِأَيۡدِيكُمۡ وَيُخۡزِهِمۡ وَيَنصُرۡكُمۡ عَلَيۡهِمۡ وَيَشۡفِ صُدُورَ قَوۡمٖ مُّؤۡمِنِينَ ﴾
[التوبَة: 14]

Amenyeni kuti Mulungu awalange iwo ndi manja anu ndi kuwachititsa manyazi, ndi kukupatsani inu kupambana ndi kuchiza mitima ya anthu okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قاتلوهم يعذبهم الله بأيديكم ويخزهم وينصركم عليهم ويشف صدور قوم مؤمنين, باللغة نيانجا

﴿قاتلوهم يعذبهم الله بأيديكم ويخزهم وينصركم عليهم ويشف صدور قوم مؤمنين﴾ [التوبَة: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Menyanani nao; Allah awalanga kupyolera m’manja anu, ndipo awasambula ndi kukupulumutsani kwa iwo ndi kuchiritsa kuwawidwa (komwe kudali) m’mitima mwa anthu okhulupirira (chifukwa cha masautso omwe adawapeza kwa iwo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek