×

Oh inu anthu okhulupirira! Kodi mwatani? Kodi ndi chifukwa chiani zimati zikanenedwa 9:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:38) ayat 38 in Chichewa

9:38 Surah At-Taubah ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 38 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مَا لَكُمۡ إِذَا قِيلَ لَكُمُ ٱنفِرُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ ٱثَّاقَلۡتُمۡ إِلَى ٱلۡأَرۡضِۚ أَرَضِيتُم بِٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا مِنَ ٱلۡأٓخِرَةِۚ فَمَا مَتَٰعُ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا فِي ٱلۡأٓخِرَةِ إِلَّا قَلِيلٌ ﴾
[التوبَة: 38]

Oh inu anthu okhulupirira! Kodi mwatani? Kodi ndi chifukwa chiani zimati zikanenedwa kwa inu kuti muyende m’njira ya Mulungu, inu mumakondweretsedwa ndi zadziko? Kodi inu mukonda moyo wa dziko lapansi kuposa moyo umene uli nkudza? Chisangalalo chadziko lapansi ndi chochepa kufanizira ndi moyo umene uli nkudza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا ما لكم إذا قيل لكم انفروا في سبيل الله, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا ما لكم إذا قيل لكم انفروا في سبيل الله﴾ [التوبَة: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Mwatani; mukauzidwa (kuti): “Pitani mukachite Jihâd pa njira ya Allah,” mukudziremetsa pa nthaka (polemedwa ndi kutulukako)? Kodi mwasangalatsidwa ndi moyo wa pa dziko lapansi kuposa moyo wa tsiku lachimaliziro? Koma zosangalatsa za m’moyo wa dziko lapansi poyerekeza ndi (moyo wa) tsiku lachimaliziro, ndi zochepa kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek