×

Kukadakhala kuti zinali zinthu zopezako mosavuta kapena ulendo waufupi, iwo akadakutsatira iwe 9:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:42) ayat 42 in Chichewa

9:42 Surah At-Taubah ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 42 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿لَوۡ كَانَ عَرَضٗا قَرِيبٗا وَسَفَرٗا قَاصِدٗا لَّٱتَّبَعُوكَ وَلَٰكِنۢ بَعُدَتۡ عَلَيۡهِمُ ٱلشُّقَّةُۚ وَسَيَحۡلِفُونَ بِٱللَّهِ لَوِ ٱسۡتَطَعۡنَا لَخَرَجۡنَا مَعَكُمۡ يُهۡلِكُونَ أَنفُسَهُمۡ وَٱللَّهُ يَعۡلَمُ إِنَّهُمۡ لَكَٰذِبُونَ ﴾
[التوبَة: 42]

Kukadakhala kuti zinali zinthu zopezako mosavuta kapena ulendo waufupi, iwo akadakutsatira iwe koma ulendo unali wautali kwa iwo ndiponso wovuta ndipo iwo akanalumbira m’dzina la Mulungu kuti: “Ife tikadatha, ndithudi, tikadapita nanu. Iwo akudziononga okha ndipo Mulungu amadziwa kuti iwo ndi abodza.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لو كان عرضا قريبا وسفرا قاصدا لاتبعوك ولكن بعدت عليهم الشقة وسيحلفون, باللغة نيانجا

﴿لو كان عرضا قريبا وسفرا قاصدا لاتبعوك ولكن بعدت عليهم الشقة وسيحلفون﴾ [التوبَة: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ukadakhala ulendo wokafuna za m’dziko zopepuka kuzipeza, ndi ulendo wofupika, ndithu akadakutsata (achiphamaso). Koma ulendo wamavutowu wakhala wautali kwa iwo. Ndipo iwo alumbilira Allah (ponena kuti): “Kukadakhala kotheka kwa ife, tikadapita nanu.” (Pa mawu awa), akudziononga okha. Ndipo Allah akudziwa kuti iwo Ngabodza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek