×

Mulungu wawalonjeza okhulupirira amuna ndi akazi, minda imene pansipake pamayenda mitsinje yamadzi, 9:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:72) ayat 72 in Chichewa

9:72 Surah At-Taubah ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 72 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿وَعَدَ ٱللَّهُ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ وَٱلۡمُؤۡمِنَٰتِ جَنَّٰتٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَا وَمَسَٰكِنَ طَيِّبَةٗ فِي جَنَّٰتِ عَدۡنٖۚ وَرِضۡوَٰنٞ مِّنَ ٱللَّهِ أَكۡبَرُۚ ذَٰلِكَ هُوَ ٱلۡفَوۡزُ ٱلۡعَظِيمُ ﴾
[التوبَة: 72]

Mulungu wawalonjeza okhulupirira amuna ndi akazi, minda imene pansipake pamayenda mitsinje yamadzi, kuti adzakhalamo mpaka kalekale ndi Nyumba zokongola za m’munda wa Edeni. Koma chisomo chachikulu ndi chisangalalo cha Mulungu. Kumeneko ndiko kupambana kweni kweni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وعد الله المؤمنين والمؤمنات جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها ومساكن, باللغة نيانجا

﴿وعد الله المؤمنين والمؤمنات جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها ومساكن﴾ [التوبَة: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah waalonjeza okhulupirira aamuna ndi okhulupirira aakazi Minda yomwe pansi (ndi patsogolo) pake mitsinje ikuyenda, adzakhala m’menemo nthawi yaitali. Ndi mokhala mwabwino m’Minda ya Edeni. Ndipo chiyanjo chochokera kwa Allah ndichachikulu (omwe ndi mtendere waukulu kwambiri kuposa zonse). Kumeneko ndiko kupambana zedi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek