×

Iwo amalumbira pali Mulungu kuti sanena china chilichonse. Koma iwo adalankhula mawu 9:74 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:74) ayat 74 in Chichewa

9:74 Surah At-Taubah ayat 74 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 74 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿يَحۡلِفُونَ بِٱللَّهِ مَا قَالُواْ وَلَقَدۡ قَالُواْ كَلِمَةَ ٱلۡكُفۡرِ وَكَفَرُواْ بَعۡدَ إِسۡلَٰمِهِمۡ وَهَمُّواْ بِمَا لَمۡ يَنَالُواْۚ وَمَا نَقَمُوٓاْ إِلَّآ أَنۡ أَغۡنَىٰهُمُ ٱللَّهُ وَرَسُولُهُۥ مِن فَضۡلِهِۦۚ فَإِن يَتُوبُواْ يَكُ خَيۡرٗا لَّهُمۡۖ وَإِن يَتَوَلَّوۡاْ يُعَذِّبۡهُمُ ٱللَّهُ عَذَابًا أَلِيمٗا فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِۚ وَمَا لَهُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ مِن وَلِيّٖ وَلَا نَصِيرٖ ﴾
[التوبَة: 74]

Iwo amalumbira pali Mulungu kuti sanena china chilichonse. Koma iwo adalankhula mawu oonetsa kusakhulupirira ndipo iwo sanakhulupirire atalowa Chisilamu. Ndipo iwo anatsimikiza kuchita zimene sadathe kuzichita. Ndipo iwo sanathe kupeza chifukwa choyenera kuti atero kupatula kuti Mulungu ndi Mtumwi wake adawalemeretsa ndi katundu wake. Ngati iwo alapa, zikhala zabwino kwa iwo, koma ngati atembenuka, ndithudi, Mulungu adzawalanga ndi chilango chowawa pa dziko lino ndi mdziko limene lili nkudza. Iwo alibe wina aliyense Wowateteza padziko lapansi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يحلفون بالله ما قالوا ولقد قالوا كلمة الكفر وكفروا بعد إسلامهم وهموا, باللغة نيانجا

﴿يحلفون بالله ما قالوا ولقد قالوا كلمة الكفر وكفروا بعد إسلامهم وهموا﴾ [التوبَة: 74]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek