×

Iwo amene adasiyidwa m’mbuyo adasangalala chifukwa cha kukhala kwawo pambuyo pa Mtumwi 9:81 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:81) ayat 81 in Chichewa

9:81 Surah At-Taubah ayat 81 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 81 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿فَرِحَ ٱلۡمُخَلَّفُونَ بِمَقۡعَدِهِمۡ خِلَٰفَ رَسُولِ ٱللَّهِ وَكَرِهُوٓاْ أَن يُجَٰهِدُواْ بِأَمۡوَٰلِهِمۡ وَأَنفُسِهِمۡ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ وَقَالُواْ لَا تَنفِرُواْ فِي ٱلۡحَرِّۗ قُلۡ نَارُ جَهَنَّمَ أَشَدُّ حَرّٗاۚ لَّوۡ كَانُواْ يَفۡقَهُونَ ﴾
[التوبَة: 81]

Iwo amene adasiyidwa m’mbuyo adasangalala chifukwa cha kukhala kwawo pambuyo pa Mtumwi wa Mulungu, iwo amadana ndi kukamenya nkhondo ndi chuma chawo ndiponsoiwoeniyokhazikitsaulamulirowa Mulungundipo iwo adati, “Musapite ku nkhondo chifukwa kuli kutentha kwambiri.” Nena, “Moto wa ku Gahena ndi wotentha kwambiri,” iwo akadangozindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فرح المخلفون بمقعدهم خلاف رسول الله وكرهوا أن يجاهدوا بأموالهم وأنفسهم في, باللغة نيانجا

﴿فرح المخلفون بمقعدهم خلاف رسول الله وكرهوا أن يجاهدوا بأموالهم وأنفسهم في﴾ [التوبَة: 81]

Khaled Ibrahim Betala
“Akondwa amene adasiidwa m’mbuyo (osapita kunkhondo) chifukwa chakukhala kwawo m’mbuyo polekana ndi Mtumiki wa Allah, nakuda kumenyana pa njira ya Allah ndi chuma chawo ndi miyoyo yawo, nati (kwa anzawo): “Musapite (ku nkhondo) m’nthawi yotenthayi.” Auze: “Moto wa Jahannam ngotentha kwambiri akadakhala akuzindikira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek