×

Kaya iwe uwapemphera chikhululukiro kapena usawapemphere, ngakhale iwe utawapemphera chikhululukiro kokwana makumi 9:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:80) ayat 80 in Chichewa

9:80 Surah At-Taubah ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 80 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿ٱسۡتَغۡفِرۡ لَهُمۡ أَوۡ لَا تَسۡتَغۡفِرۡ لَهُمۡ إِن تَسۡتَغۡفِرۡ لَهُمۡ سَبۡعِينَ مَرَّةٗ فَلَن يَغۡفِرَ ٱللَّهُ لَهُمۡۚ ذَٰلِكَ بِأَنَّهُمۡ كَفَرُواْ بِٱللَّهِ وَرَسُولِهِۦۗ وَٱللَّهُ لَا يَهۡدِي ٱلۡقَوۡمَ ٱلۡفَٰسِقِينَ ﴾
[التوبَة: 80]

Kaya iwe uwapemphera chikhululukiro kapena usawapemphere, ngakhale iwe utawapemphera chikhululukiro kokwana makumi asanu ndi awiri, Mulungu sadzawakhululukira chifukwa iwo sanakhulupilire mwa Mulungu ndi Mtumwi wake. Ndipo Mulungu satsogolera anthu ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: استغفر لهم أو لا تستغفر لهم إن تستغفر لهم سبعين مرة فلن, باللغة نيانجا

﴿استغفر لهم أو لا تستغفر لهم إن تستغفر لهم سبعين مرة فلن﴾ [التوبَة: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“(E iwe Mtumiki!) Uwapemphere chikhululuko (achiphamaso) kapena usawapemphere, (zonsezo nchimodzimodzi). Ngakhale utawapemphera chikhululuko chochuluka kwabasi mokwanira makumi asanu ndi awiri Allah sangawakhululukire. Zimenezo nchifukwa chakuti iwo amkana Allah ndi Mtumiki Wake. Ndipo Allah satsogolera anthu ophwanya malamulo (Ake)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek