×

Iwo adzalumbira kwa inu M’dzina la Mulungu pamene mubwerera kwa iwo kuti 9:95 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:95) ayat 95 in Chichewa

9:95 Surah At-Taubah ayat 95 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 95 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿سَيَحۡلِفُونَ بِٱللَّهِ لَكُمۡ إِذَا ٱنقَلَبۡتُمۡ إِلَيۡهِمۡ لِتُعۡرِضُواْ عَنۡهُمۡۖ فَأَعۡرِضُواْ عَنۡهُمۡۖ إِنَّهُمۡ رِجۡسٞۖ وَمَأۡوَىٰهُمۡ جَهَنَّمُ جَزَآءَۢ بِمَا كَانُواْ يَكۡسِبُونَ ﴾
[التوبَة: 95]

Iwo adzalumbira kwa inu M’dzina la Mulungu pamene mubwerera kwa iwo kuti muwasiye okha. Motero asiyeni okha chifukwa iwo ndi uve chifukwa cha ntchito zawo. Ndipo yawo ndi Gahena, omwe ndi malipiro antchito zimene ankachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: سيحلفون بالله لكم إذا انقلبتم إليهم لتعرضوا عنهم فأعرضوا عنهم إنهم رجس, باللغة نيانجا

﴿سيحلفون بالله لكم إذا انقلبتم إليهم لتعرضوا عنهم فأعرضوا عنهم إنهم رجس﴾ [التوبَة: 95]

Khaled Ibrahim Betala
“Mukabwerera kwa iwo, adzalumbira m’dzina la Allah kwa inu kuti muwasiye (musawachite kanthu). Choncho, apatukireni. Ndithu iwo ndiuve ndipo malo awo ndi ku Jahannam. Iyi ndi mphoto ya zomwe adali kupeza (kuchokera m’zochita zawo zoipa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek