×

Iwo amene sakhulupirira a m’gulu la anthu a m’Buku ndi anthu opembedza 98:1 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Bayyinah ⮕ (98:1) ayat 1 in Chichewa

98:1 Surah Al-Bayyinah ayat 1 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Bayyinah ayat 1 - البَينَة - Page - Juz 30

﴿لَمۡ يَكُنِ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ مِنۡ أَهۡلِ ٱلۡكِتَٰبِ وَٱلۡمُشۡرِكِينَ مُنفَكِّينَ حَتَّىٰ تَأۡتِيَهُمُ ٱلۡبَيِّنَةُ ﴾
[البَينَة: 1]

Iwo amene sakhulupirira a m’gulu la anthu a m’Buku ndi anthu opembedza mafano, sadzasiya kusakhulupilira mpaka pamene zizindikiro zooneka zitaperekedwa kwa iwo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لم يكن الذين كفروا من أهل الكتاب والمشركين منفكين حتى تأتيهم البينة, باللغة نيانجا

﴿لم يكن الذين كفروا من أهل الكتاب والمشركين منفكين حتى تأتيهم البينة﴾ [البَينَة: 1]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene adakanira (Allah ndi Mthenga Wake) mwa omwe adapatsidwa buku ndi opembedza mafano sadali olekana (ndi umbuli wawo ndi kusalabadira kwawo choona) mpaka pomwe chidawadzera chisonyezo choonekera poyera
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek