×

Nena, “oh inu anthu! Ngati inu muli ndi chikaiko pa chipembedzo changa, 10:104 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:104) ayat 104 in Chichewa

10:104 Surah Yunus ayat 104 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 104 - يُونس - Page - Juz 11

﴿قُلۡ يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّاسُ إِن كُنتُمۡ فِي شَكّٖ مِّن دِينِي فَلَآ أَعۡبُدُ ٱلَّذِينَ تَعۡبُدُونَ مِن دُونِ ٱللَّهِ وَلَٰكِنۡ أَعۡبُدُ ٱللَّهَ ٱلَّذِي يَتَوَفَّىٰكُمۡۖ وَأُمِرۡتُ أَنۡ أَكُونَ مِنَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[يُونس: 104]

Nena, “oh inu anthu! Ngati inu muli ndi chikaiko pa chipembedzo changa, dziwani kuti ine sindidzapembedza zomwe mukuzipembedza kuonjezera pa Mulungu weniweni. Koma ine ndikupembedza Mulungu amene amakuphani nonse ndipo ndalamulidwa kuti ndikhale mmodzi wa anthu okhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل ياأيها الناس إن كنتم في شك من ديني فلا أعبد الذين, باللغة نيانجا

﴿قل ياأيها الناس إن كنتم في شك من ديني فلا أعبد الذين﴾ [يُونس: 104]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “E inu anthu! Ngati inu muli ndi chipeneko pa chipembedzo changa, (dziwani kuti) sindingapembedze zimene mukuzipembedza kusiya Allah; koma ine ndipembedza Allah (Mmodzi yekha) Yemwe amakupatsani imfa (ndi moyo). Ndipo ndalamulidwa kukhala mmodzi wa okhulupirira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek