×

Ndipo usapembedze wina aliyense yemwe si Mulungu, amene sangathe kukuthandiza kapena kukuononga 10:106 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:106) ayat 106 in Chichewa

10:106 Surah Yunus ayat 106 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 106 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَلَا تَدۡعُ مِن دُونِ ٱللَّهِ مَا لَا يَنفَعُكَ وَلَا يَضُرُّكَۖ فَإِن فَعَلۡتَ فَإِنَّكَ إِذٗا مِّنَ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[يُونس: 106]

Ndipo usapembedze wina aliyense yemwe si Mulungu, amene sangathe kukuthandiza kapena kukuononga chifukwa, utatero, udzakhala mmodzi wa wochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا تدع من دون الله ما لا ينفعك ولا يضرك فإن فعلت, باللغة نيانجا

﴿ولا تدع من دون الله ما لا ينفعك ولا يضرك فإن فعلت﴾ [يُونس: 106]

Khaled Ibrahim Betala
“‘Ndipo (kuti), usapembedze chimene sichingakupindulitsire zabwino, kapena kukubweretsera masautso, kusiya Allah. Ngati utero ndiye kuti iwe ndi mmodzi wa oipa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek