×

Nena, “Ine ndilibe mphamvu yopeza zabwino kapena kupewa choipa chimene chingadze pa 10:49 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:49) ayat 49 in Chichewa

10:49 Surah Yunus ayat 49 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 49 - يُونس - Page - Juz 11

﴿قُل لَّآ أَمۡلِكُ لِنَفۡسِي ضَرّٗا وَلَا نَفۡعًا إِلَّا مَا شَآءَ ٱللَّهُۗ لِكُلِّ أُمَّةٍ أَجَلٌۚ إِذَا جَآءَ أَجَلُهُمۡ فَلَا يَسۡتَـٔۡخِرُونَ سَاعَةٗ وَلَا يَسۡتَقۡدِمُونَ ﴾
[يُونس: 49]

Nena, “Ine ndilibe mphamvu yopeza zabwino kapena kupewa choipa chimene chingadze pa ine kupatula ndi chifuniro cha Mulungu. M’badwo uliwonse uli ndi nthawi imene idakhazikitsidwa kale. Ndipo pamene nthawi yawo idza, iwo sadzatha kuichedwetsa kapena kuifulumizitsa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل لا أملك لنفسي ضرا ولا نفعا إلا ما شاء الله لكل, باللغة نيانجا

﴿قل لا أملك لنفسي ضرا ولا نفعا إلا ما شاء الله لكل﴾ [يُونس: 49]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ndilibe mphamvu mwandekha pa (kudzichotsera) vuto ngakhale (kudzibweretsera) thandizo. (Nanga za zimenezo ndingadziweponji)? Koma chimene Allah wafuna (ndi chomwe chimachitika). M’badwo uli wonse uli ndi nthawi yake (yofera). Nthawi yawo (yofera) ikadza sangathe kuichedwetsa ola limodzi ngakhale kuifulumizitsa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek