×

Akakhala anthu odala, iwo adzakhala ku Paradiso mpaka pamene kumwamba ndi dziko 11:108 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:108) ayat 108 in Chichewa

11:108 Surah Hud ayat 108 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 108 - هُود - Page - Juz 12

﴿۞ وَأَمَّا ٱلَّذِينَ سُعِدُواْ فَفِي ٱلۡجَنَّةِ خَٰلِدِينَ فِيهَا مَا دَامَتِ ٱلسَّمَٰوَٰتُ وَٱلۡأَرۡضُ إِلَّا مَا شَآءَ رَبُّكَۖ عَطَآءً غَيۡرَ مَجۡذُوذٖ ﴾
[هُود: 108]

Akakhala anthu odala, iwo adzakhala ku Paradiso mpaka pamene kumwamba ndi dziko lapansi zidzakhale zilipobe kupatula ngati Ambuye wako afuna kusintha, mphatso yosatha mpaka kalekale

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأما الذين سعدوا ففي الجنة خالدين فيها ما دامت السموات والأرض إلا, باللغة نيانجا

﴿وأما الذين سعدوا ففي الجنة خالدين فيها ما دامت السموات والأرض إلا﴾ [هُود: 108]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsono amene adzakhale abwino adzakhala m’Munda wamtendere. Adzakhala mmenemo nthawi yaitali momwe thambo ndi nthaka zidzakhalire, kupatula Mbuye wako akadzafuna; zopatsa (za Mbuye wako ndizo zopatsa) zosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek