×

Kupatula yekhayo amene Ambuye wako wamuonetsera chisomo chake ndipo ndicho chifukwa chake 11:119 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:119) ayat 119 in Chichewa

11:119 Surah Hud ayat 119 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 119 - هُود - Page - Juz 12

﴿إِلَّا مَن رَّحِمَ رَبُّكَۚ وَلِذَٰلِكَ خَلَقَهُمۡۗ وَتَمَّتۡ كَلِمَةُ رَبِّكَ لَأَمۡلَأَنَّ جَهَنَّمَ مِنَ ٱلۡجِنَّةِ وَٱلنَّاسِ أَجۡمَعِينَ ﴾
[هُود: 119]

Kupatula yekhayo amene Ambuye wako wamuonetsera chisomo chake ndipo ndicho chifukwa chake chimene Mulungu adawalengera. Mawu a Ambuye wako adzakwaniritsidwa “Ndithudi Ine ndidzadzadza Gahena ndi Majini ndi anthu onse pamodzi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إلا من رحم ربك ولذلك خلقهم وتمت كلمة ربك لأملأن جهنم من, باللغة نيانجا

﴿إلا من رحم ربك ولذلك خلقهم وتمت كلمة ربك لأملأن جهنم من﴾ [هُود: 119]

Khaled Ibrahim Betala
“Kupatula omwe Mbuye wako wawachitira chifundo; ndipo chifukwa cha chifundocho, adawalenga (koma okha akusankha zoipa). Ndipo mawu a Mbuye wako akwaniritsidwa (akuti): “Ndithudi, ndizadzadzitsa Jahannam ndi ziwanda ndi anthu onse pamodzi (omwe adali oipa).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek