×

Aliyense amene afuna moyo wa m’dziko lino pamodzi ndi zokondweretsa zake, Ife 11:15 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:15) ayat 15 in Chichewa

11:15 Surah Hud ayat 15 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 15 - هُود - Page - Juz 12

﴿مَن كَانَ يُرِيدُ ٱلۡحَيَوٰةَ ٱلدُّنۡيَا وَزِينَتَهَا نُوَفِّ إِلَيۡهِمۡ أَعۡمَٰلَهُمۡ فِيهَا وَهُمۡ فِيهَا لَا يُبۡخَسُونَ ﴾
[هُود: 15]

Aliyense amene afuna moyo wa m’dziko lino pamodzi ndi zokondweretsa zake, Ife tidzawalipira molingana ndi ntchito zawo , mopanda kuchotsera chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من كان يريد الحياة الدنيا وزينتها نوف إليهم أعمالهم فيها وهم فيها, باللغة نيانجا

﴿من كان يريد الحياة الدنيا وزينتها نوف إليهم أعمالهم فيها وهم فيها﴾ [هُود: 15]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene akufuna moyo wa dziko lapansi ndi zokometsera zake, tiwapatsa pompo pa dziko lapansi (malipiro a) zochita zawo mokwanira, ndipo iwo m’menemo sachepetseredwa chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek