×

Mkazi uja adati, “Uyu ndiye mnyamata uja amene nonsenu munali kundidzudzula naye. 12:32 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:32) ayat 32 in Chichewa

12:32 Surah Yusuf ayat 32 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 32 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿قَالَتۡ فَذَٰلِكُنَّ ٱلَّذِي لُمۡتُنَّنِي فِيهِۖ وَلَقَدۡ رَٰوَدتُّهُۥ عَن نَّفۡسِهِۦ فَٱسۡتَعۡصَمَۖ وَلَئِن لَّمۡ يَفۡعَلۡ مَآ ءَامُرُهُۥ لَيُسۡجَنَنَّ وَلَيَكُونٗا مِّنَ ٱلصَّٰغِرِينَ ﴾
[يُوسُف: 32]

Mkazi uja adati, “Uyu ndiye mnyamata uja amene nonsenu munali kundidzudzula naye. Ndithudi ine ndidamunyenga koma iye adakanitsitsa. Tsopano ngati iye sachita zimene ndikumulamulira, ndithudi, adzaponyedwa ku ndende ndipo adzakhala mmodziwaanthuonyozedwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالت فذلكن الذي لمتنني فيه ولقد راودته عن نفسه فاستعصم ولئن لم, باللغة نيانجا

﴿قالت فذلكن الذي لمتنني فيه ولقد راودته عن نفسه فاستعصم ولئن لم﴾ [يُوسُف: 32]

Khaled Ibrahim Betala
“(Mkazi wa nduna) adati: “Uyu ndi amene mumandidzudzula naye. Ndithudi ndidamulakalaka pomwe iye samandifuna ndipo anadziteteza. Ndipo ngati sachita chimene ndikumulamula, ndithu amangidwa ndipo ndithu akhala m’gulu la onyozeka!”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek