×

Ndipo anyamata awiri adalowa m’ndende pamodzi ndi iye. Mmodzi wa iwo adati, 12:36 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:36) ayat 36 in Chichewa

12:36 Surah Yusuf ayat 36 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 36 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿وَدَخَلَ مَعَهُ ٱلسِّجۡنَ فَتَيَانِۖ قَالَ أَحَدُهُمَآ إِنِّيٓ أَرَىٰنِيٓ أَعۡصِرُ خَمۡرٗاۖ وَقَالَ ٱلۡأٓخَرُ إِنِّيٓ أَرَىٰنِيٓ أَحۡمِلُ فَوۡقَ رَأۡسِي خُبۡزٗا تَأۡكُلُ ٱلطَّيۡرُ مِنۡهُۖ نَبِّئۡنَا بِتَأۡوِيلِهِۦٓۖ إِنَّا نَرَىٰكَ مِنَ ٱلۡمُحۡسِنِينَ ﴾
[يُوسُف: 36]

Ndipo anyamata awiri adalowa m’ndende pamodzi ndi iye. Mmodzi wa iwo adati, “Ndithudi ine ndalota ndili kutcheza vinyo” Ndipo wina adanena kuti, “Ine ndinalota nditanyamula pamutu panga mkate umene mbalame zimadya. Tiuze matanthauzo ake. Ndithudi ife tikukuona iwe kuti uli mmodzi wa anthu wochita zabwino.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ودخل معه السجن فتيان قال أحدهما إني أراني أعصر خمرا وقال الآخر, باللغة نيانجا

﴿ودخل معه السجن فتيان قال أحدهما إني أراني أعصر خمرا وقال الآخر﴾ [يُوسُف: 36]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo anyamata awiri adalowa m’ndende pamodzi ndi iye. Mmodzi mwa iwo adati (kumuuza Yûsuf): “Ndithu ine ndalota ndikufulula mowa.” Ndipo wina adati: “Ndithu ine ndalota ndikusenza mikate pamutu panga yomwe idali kudyedwa ndi mbalame. Tiuze tanthauzo lake. Ndithu ife tikukuona iwe kuti ndiwe mmodzi wa anthu abwino.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek