×

Iwo adati: “Aliyense amene m’thumba mwake mupezeke mbale, iyeyo ndiye adzalandira chilango 12:75 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:75) ayat 75 in Chichewa

12:75 Surah Yusuf ayat 75 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 75 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿قَالُواْ جَزَٰٓؤُهُۥ مَن وُجِدَ فِي رَحۡلِهِۦ فَهُوَ جَزَٰٓؤُهُۥۚ كَذَٰلِكَ نَجۡزِي ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[يُوسُف: 75]

Iwo adati: “Aliyense amene m’thumba mwake mupezeke mbale, iyeyo ndiye adzalandira chilango cha mbaleyo. Kotero ndimo mmene ife timalangira athu ochita zoipa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالوا جزاؤه من وجد في رحله فهو جزاؤه كذلك نجزي الظالمين, باللغة نيانجا

﴿قالوا جزاؤه من وجد في رحله فهو جزاؤه كذلك نجزي الظالمين﴾ [يُوسُف: 75]

Khaled Ibrahim Betala
“Adati: “Mphoto yake ndi yemwe (chikhocho) chapezeka mu mtolo wake, iye ndiye mphoto yake. (Agwidwe monga kapolo kwa chaka chimodzi).” Umu ndi momwe timawalipirira anthu achinyengo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek