×

Ndipo iye adayang’ana kumbali nati, “Kalanga! Ine ndili ndi chisoni ndi Yosefe!” 12:84 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:84) ayat 84 in Chichewa

12:84 Surah Yusuf ayat 84 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 84 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿وَتَوَلَّىٰ عَنۡهُمۡ وَقَالَ يَٰٓأَسَفَىٰ عَلَىٰ يُوسُفَ وَٱبۡيَضَّتۡ عَيۡنَاهُ مِنَ ٱلۡحُزۡنِ فَهُوَ كَظِيمٞ ﴾
[يُوسُف: 84]

Ndipo iye adayang’ana kumbali nati, “Kalanga! Ine ndili ndi chisoni ndi Yosefe!” Maso ake adachita khungu chifukwachachisonichachikuluchimenechinalimumtima mwake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وتولى عنهم وقال ياأسفى على يوسف وابيضت عيناه من الحزن فهو كظيم, باللغة نيانجا

﴿وتولى عنهم وقال ياأسفى على يوسف وابيضت عيناه من الحزن فهو كظيم﴾ [يُوسُف: 84]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo adawachokera ndikunena (kuti): “Ha! kudandaula kwanga za Yûsuf!” Ndipo maso ake adayera chifukwa cha kudandaula ndipo iye adadzazidwa ndi chisoni
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek