×

Ife tili kudziwa kwambiri zimene adzayankhula, pamene anthu awo angwiro ndi anzeru 20:104 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:104) ayat 104 in Chichewa

20:104 Surah Ta-Ha ayat 104 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 104 - طه - Page - Juz 16

﴿نَّحۡنُ أَعۡلَمُ بِمَا يَقُولُونَ إِذۡ يَقُولُ أَمۡثَلُهُمۡ طَرِيقَةً إِن لَّبِثۡتُمۡ إِلَّا يَوۡمٗا ﴾
[طه: 104]

Ife tili kudziwa kwambiri zimene adzayankhula, pamene anthu awo angwiro ndi anzeru adzati, “Inu simunakhale padziko kupatula tsiku limodzi lokha.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: نحن أعلم بما يقولون إذ يقول أمثلهم طريقة إن لبثتم إلا يوما, باللغة نيانجا

﴿نحن أعلم بما يقولون إذ يقول أمثلهم طريقة إن لبثتم إلا يوما﴾ [طه: 104]

Khaled Ibrahim Betala
“Ife tikudziwa kwambiri zimene azidzanena pamene abwino awo pamayendedwe azidzanena: “Inu simudakhale koma tsiku limodzi basi (poyerekeza ndi kuchuluka kwa masiku a ku Moto).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek