×

Oh inu anthu okhulupirira! Musalowe m’nyumba za anthu ena pokhapokha mutapempha chilolezo 24:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:27) ayat 27 in Chichewa

24:27 Surah An-Nur ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 27 - النور - Page - Juz 18

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَا تَدۡخُلُواْ بُيُوتًا غَيۡرَ بُيُوتِكُمۡ حَتَّىٰ تَسۡتَأۡنِسُواْ وَتُسَلِّمُواْ عَلَىٰٓ أَهۡلِهَاۚ ذَٰلِكُمۡ خَيۡرٞ لَّكُمۡ لَعَلَّكُمۡ تَذَكَّرُونَ ﴾
[النور: 27]

Oh inu anthu okhulupirira! Musalowe m’nyumba za anthu ena pokhapokha mutapempha chilolezo cha eni ake ndipo alonjereni powafunira iwo mtendere. Zimenezo ndi zabwino kwa inu kuti muchenjezedwe

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا لا تدخلوا بيوتا غير بيوتكم حتى تستأنسوا وتسلموا على, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا لا تدخلوا بيوتا غير بيوتكم حتى تستأنسوا وتسلموا على﴾ [النور: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Musalowe m’nyumba zomwe sinyumba zanu kufikira mutapempha chilolezo poodira ndikupereka Salaam kwa eni nyumbazo. Kutero ndi kwa bwino kwa inu kuti mukumbukire (nkuona kuti zomwe mukuuzidwa nzabwino)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek