×

Mukapeza kuti kulibe aliyense, musalowe mpaka pokhapokha mwapatsidwa chilolezo. Ngati akuuzani kuti 24:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:28) ayat 28 in Chichewa

24:28 Surah An-Nur ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 28 - النور - Page - Juz 18

﴿فَإِن لَّمۡ تَجِدُواْ فِيهَآ أَحَدٗا فَلَا تَدۡخُلُوهَا حَتَّىٰ يُؤۡذَنَ لَكُمۡۖ وَإِن قِيلَ لَكُمُ ٱرۡجِعُواْ فَٱرۡجِعُواْۖ هُوَ أَزۡكَىٰ لَكُمۡۚ وَٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ عَلِيمٞ ﴾
[النور: 28]

Mukapeza kuti kulibe aliyense, musalowe mpaka pokhapokha mwapatsidwa chilolezo. Ngati akuuzani kuti mubwerere kapena musalowe, ndi chilungamo kuti inu mubwerere kupita komwe mwachokera. Zimenezo ndi zabwino kwa inu. Mulungu amadziwa zonse zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن لم تجدوا فيها أحدا فلا تدخلوها حتى يؤذن لكم وإن قيل, باللغة نيانجا

﴿فإن لم تجدوا فيها أحدا فلا تدخلوها حتى يؤذن لكم وإن قيل﴾ [النور: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma ngati simupeza munthu aliyense m’menemo, musalowe kufikira mutapatsidwa chilolezo. Ndipo mukauzidwa kuti: “Bwererani.” Bwererani; chimenechi nchokuyeretsani. Ndipo Allah akudziwa zimene muchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek