×

Nena “Mverani Mulungu ndipo mverani Mtumwi wake. Ngati simungamvere, iye ali ndi 24:54 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:54) ayat 54 in Chichewa

24:54 Surah An-Nur ayat 54 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 54 - النور - Page - Juz 18

﴿قُلۡ أَطِيعُواْ ٱللَّهَ وَأَطِيعُواْ ٱلرَّسُولَۖ فَإِن تَوَلَّوۡاْ فَإِنَّمَا عَلَيۡهِ مَا حُمِّلَ وَعَلَيۡكُم مَّا حُمِّلۡتُمۡۖ وَإِن تُطِيعُوهُ تَهۡتَدُواْۚ وَمَا عَلَى ٱلرَّسُولِ إِلَّا ٱلۡبَلَٰغُ ٱلۡمُبِينُ ﴾
[النور: 54]

Nena “Mverani Mulungu ndipo mverani Mtumwi wake. Ngati simungamvere, iye ali ndi udindo wake monga momwe inu muli ndi udindo wanu. Ngati inu mumumvera, inu mudzatsogozedwa ndipo udindo wa Mtumwi ndi kungopereka uthenga womveka.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل أطيعوا الله وأطيعوا الرسول فإن تولوا فإنما عليه ما حمل وعليكم, باللغة نيانجا

﴿قل أطيعوا الله وأطيعوا الرسول فإن تولوا فإنما عليه ما حمل وعليكم﴾ [النور: 54]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Mverani Allah, ndiponso Mverani Mtumiki. Koma ngati mutembenuka, iye ali nazo zimene wasenzetsedwa (kuti azifikitse kwa inu), (ndipo) inunso muli nazo zimene mwasenzetsedwa (kuti muzitsate). Ndipo mukamumvera, muongoka. Ndipo pa Mtumiki palibe china chake koma kufikitsa (uthenga) momveka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek