×

Ndipo Ambuye wako sadaononge mizinda mpaka pamene Iye adadzutsa kuchokera mu iyo, 28:59 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:59) ayat 59 in Chichewa

28:59 Surah Al-Qasas ayat 59 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 59 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَمَا كَانَ رَبُّكَ مُهۡلِكَ ٱلۡقُرَىٰ حَتَّىٰ يَبۡعَثَ فِيٓ أُمِّهَا رَسُولٗا يَتۡلُواْ عَلَيۡهِمۡ ءَايَٰتِنَاۚ وَمَا كُنَّا مُهۡلِكِي ٱلۡقُرَىٰٓ إِلَّا وَأَهۡلُهَا ظَٰلِمُونَ ﴾
[القَصَص: 59]

Ndipo Ambuye wako sadaononge mizinda mpaka pamene Iye adadzutsa kuchokera mu iyo, Mtumwi amene amalalikira za chivumbulutso chathu ndipo Ife sitidzaononga mzinda pokhapokha anthu okhala mmenemo ali olakwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان ربك مهلك القرى حتى يبعث في أمها رسولا يتلو عليهم, باللغة نيانجا

﴿وما كان ربك مهلك القرى حتى يبعث في أمها رسولا يتلو عليهم﴾ [القَصَص: 59]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Mbuye wako sali owononga midzi pokhapokha akatuma mtumiki mu mzinda wawo waukulu ndi kuwawerengera mawu a m’ndime Zathu, (akakana ndi pamene timawaononga); ndiponso sitili owononga midzi pokhapokha anthu ake atakhala achinyengo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek