×

Ndipo iwo sadanene china koma kuti: “oh Ambuye! Tikhululukireni machimo athu ndi 3:147 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:147) ayat 147 in Chichewa

3:147 Surah al-‘Imran ayat 147 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 147 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَمَا كَانَ قَوۡلَهُمۡ إِلَّآ أَن قَالُواْ رَبَّنَا ٱغۡفِرۡ لَنَا ذُنُوبَنَا وَإِسۡرَافَنَا فِيٓ أَمۡرِنَا وَثَبِّتۡ أَقۡدَامَنَا وَٱنصُرۡنَا عَلَى ٱلۡقَوۡمِ ٱلۡكَٰفِرِينَ ﴾
[آل عِمران: 147]

Ndipo iwo sadanene china koma kuti: “oh Ambuye! Tikhululukireni machimo athu ndi kuswa malamulo kwathu. Limbikitsani mapazi athu ndipo tipambanitseni kwa anthu osakhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان قولهم إلا أن قالوا ربنا اغفر لنا ذنوبنا وإسرافنا في, باللغة نيانجا

﴿وما كان قولهم إلا أن قالوا ربنا اغفر لنا ذنوبنا وإسرافنا في﴾ [آل عِمران: 147]

Khaled Ibrahim Betala
“(Anthu olungamawa) kunena kwawo sikudali kwina koma ankati: “Mbuye wathu! Tikhululukireni machimo athu ndi kupyola malire kwathu m’zinthu zathu. Ndipo limbikitsani mapazi athu (panjira Yanu) ndipo tithandizeni ku anthu osakhulupirira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek