×

Pamene inu mudathawa osaona kumbali kwa wina aliyense ndipo Mtumwi adali m’mbuyo 3:153 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:153) ayat 153 in Chichewa

3:153 Surah al-‘Imran ayat 153 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 153 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿۞ إِذۡ تُصۡعِدُونَ وَلَا تَلۡوُۥنَ عَلَىٰٓ أَحَدٖ وَٱلرَّسُولُ يَدۡعُوكُمۡ فِيٓ أُخۡرَىٰكُمۡ فَأَثَٰبَكُمۡ غَمَّۢا بِغَمّٖ لِّكَيۡلَا تَحۡزَنُواْ عَلَىٰ مَا فَاتَكُمۡ وَلَا مَآ أَصَٰبَكُمۡۗ وَٱللَّهُ خَبِيرُۢ بِمَا تَعۡمَلُونَ ﴾
[آل عِمران: 153]

Pamene inu mudathawa osaona kumbali kwa wina aliyense ndipo Mtumwi adali m’mbuyo mwanu kukuitanani. Pamenepo Mulungu anakupatsani vuto powonjezera pa vuto lina ngati kubwezera ndi cholinga chokuphunzitsani inu kuti musamve chisoni pa zimene simunazipeze kapena zimene zinadza kwa inu. Mulungu amadziwa zonse zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ تصعدون ولا تلوون على أحد والرسول يدعوكم في أخراكم فأثابكم غما, باللغة نيانجا

﴿إذ تصعدون ولا تلوون على أحد والرسول يدعوكم في أخراكم فأثابكم غما﴾ [آل عِمران: 153]

Khaled Ibrahim Betala
“Kumbukirani pamene mudali kuthawa mwa liwiro popanda kumvera aliyense; pomwe Mtumiki adali kukuitanani, ali pambuyo panu. Ndipo (Allah) Adakupatsani madandaulo pa madandaulo. (Motero wakukhululukirani) kuti musadandaule pa zomwe zakudutsani, ngakhalenso (pa masautso) omwe akupezani. Ndipo Allah Ngodziwa zonse zimene muchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek