×

Ndipo asakukhumudwitseni anthu amene amachita changu posakhulupirira. Ndithudi iwo sangachite chili chonse 3:176 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:176) ayat 176 in Chichewa

3:176 Surah al-‘Imran ayat 176 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 176 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَلَا يَحۡزُنكَ ٱلَّذِينَ يُسَٰرِعُونَ فِي ٱلۡكُفۡرِۚ إِنَّهُمۡ لَن يَضُرُّواْ ٱللَّهَ شَيۡـٔٗاۚ يُرِيدُ ٱللَّهُ أَلَّا يَجۡعَلَ لَهُمۡ حَظّٗا فِي ٱلۡأٓخِرَةِۖ وَلَهُمۡ عَذَابٌ عَظِيمٌ ﴾
[آل عِمران: 176]

Ndipo asakukhumudwitseni anthu amene amachita changu posakhulupirira. Ndithudi iwo sangachite chili chonse chomupweteka Mulungu. Ndi cholinga cha Mulungu kuti iwo asadzapatsidwe gawo lina lililonse m’moyo umene uli nkudza. Iwo ali ndi chilango chachikulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا يحزنك الذين يسارعون في الكفر إنهم لن يضروا الله شيئا يريد, باللغة نيانجا

﴿ولا يحزنك الذين يسارعون في الكفر إنهم لن يضروا الله شيئا يريد﴾ [آل عِمران: 176]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo asakudandaulitse omwe akuthamangira kuchita zinthu zachikunja. Ndithu iwo sangapereke sautso lililonse kwa Allah. Allah akufuna kuti asawaikire gawo lililonse la (zabwino) tsiku lachimaliziro, ndipo pa iwo padzakhala chilango chachikulu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek