×

Pamene mkazi wa Imran adati: “Ambuye wanga! Ine ndilonjeza kwa Inu chinthu 3:35 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:35) ayat 35 in Chichewa

3:35 Surah al-‘Imran ayat 35 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 35 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿إِذۡ قَالَتِ ٱمۡرَأَتُ عِمۡرَٰنَ رَبِّ إِنِّي نَذَرۡتُ لَكَ مَا فِي بَطۡنِي مُحَرَّرٗا فَتَقَبَّلۡ مِنِّيٓۖ إِنَّكَ أَنتَ ٱلسَّمِيعُ ٱلۡعَلِيمُ ﴾
[آل عِمران: 35]

Pamene mkazi wa Imran adati: “Ambuye wanga! Ine ndilonjeza kwa Inu chinthu chimene chili m’mimba mwanga kuti chidzakhale chokutumikirani Inu. Motero landirani ichi kuchokera kwa ine ngati nsembe yanga. Ndithudi Inu ndinu wakumva ndi wozindikira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ قالت امرأة عمران رب إني نذرت لك ما في بطني محررا, باللغة نيانجا

﴿إذ قالت امرأة عمران رب إني نذرت لك ما في بطني محررا﴾ [آل عِمران: 35]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukirani) pamene adanena mkazi wa Imran (mayi wa Mariya), m’mapemphero ake): “Mbuye wanga! Ndapereka kwa Inu chimene chili m’mimba mwanga monga “waqf” (wotumikira m’kachisi Wanu). Tero landirani ichi kwa ine. Ndithudi, Inu ndinu Akumva, Wodziwa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek