×

Ndipo pamene iye anabereka mwana wake, iye adati: “Ambuye wanga! Ine ndabereka 3:36 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:36) ayat 36 in Chichewa

3:36 Surah al-‘Imran ayat 36 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 36 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿فَلَمَّا وَضَعَتۡهَا قَالَتۡ رَبِّ إِنِّي وَضَعۡتُهَآ أُنثَىٰ وَٱللَّهُ أَعۡلَمُ بِمَا وَضَعَتۡ وَلَيۡسَ ٱلذَّكَرُ كَٱلۡأُنثَىٰۖ وَإِنِّي سَمَّيۡتُهَا مَرۡيَمَ وَإِنِّيٓ أُعِيذُهَا بِكَ وَذُرِّيَّتَهَا مِنَ ٱلشَّيۡطَٰنِ ٱلرَّجِيمِ ﴾
[آل عِمران: 36]

Ndipo pamene iye anabereka mwana wake, iye adati: “Ambuye wanga! Ine ndabereka mwana wamkazi.” Koma Mulungu anadziwiratu chimene iye wabereka. “Ndipo mwana wamwamuna salingana ndi mwana wa mkazi, ndipo ine ndamutcha dzina la Maria ndipo ndili kumupereka iye pamodzi ndi mbewu yake kwa Inu kuti muwateteze kwa Satana wotembereredwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما وضعتها قالت رب إني وضعتها أنثى والله أعلم بما وضعت وليس, باللغة نيانجا

﴿فلما وضعتها قالت رب إني وضعتها أنثى والله أعلم بما وضعت وليس﴾ [آل عِمران: 36]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho pamene adam’bala adati: “Mbuye wanga! Ndabala wamkazi!” Ndipo Allah akudziwa kwambiri chimene wabereka - “Ndipo wamwamuna (yemwe ndimayembekezera kubala) sali ngati wamkazi (amene ndamubala. Sangathe kutumikira moyenera mkachisi Wanu). Ndipo ine ndamutcha Mariya (wotumikira Allah). Ndipo ndikupempha Chitetezo Chanu pa iye ndi ana ake kwa satana wothamangitsidwayo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek