×

Ndi pamene angelo adati: “oh Maria! Ndithudi Mulungu wakusankha ndi kukuyeretsa iwe 3:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:42) ayat 42 in Chichewa

3:42 Surah al-‘Imran ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 42 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿وَإِذۡ قَالَتِ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةُ يَٰمَرۡيَمُ إِنَّ ٱللَّهَ ٱصۡطَفَىٰكِ وَطَهَّرَكِ وَٱصۡطَفَىٰكِ عَلَىٰ نِسَآءِ ٱلۡعَٰلَمِينَ ﴾
[آل عِمران: 42]

Ndi pamene angelo adati: “oh Maria! Ndithudi Mulungu wakusankha ndi kukuyeretsa iwe ndipo wakusankha kukhala wapamwamba pakati pa akazi ena a zolengedwa zonse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ قالت الملائكة يامريم إن الله اصطفاك وطهرك واصطفاك على نساء العالمين, باللغة نيانجا

﴿وإذ قالت الملائكة يامريم إن الله اصطفاك وطهرك واصطفاك على نساء العالمين﴾ [آل عِمران: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbukira) pamene angelo adati: “E Iwe Mariya! Ndithudi, Allah wakusankha, wakuyeretsa ndipo wakulemekeza, mwa akazi onse amitundu ya anthu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek