×

Ndipo pamene Yesu adaona kuti iwo adalibe chikhulupiriro, iye adati: “Kodi ndani 3:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:52) ayat 52 in Chichewa

3:52 Surah al-‘Imran ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 52 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿۞ فَلَمَّآ أَحَسَّ عِيسَىٰ مِنۡهُمُ ٱلۡكُفۡرَ قَالَ مَنۡ أَنصَارِيٓ إِلَى ٱللَّهِۖ قَالَ ٱلۡحَوَارِيُّونَ نَحۡنُ أَنصَارُ ٱللَّهِ ءَامَنَّا بِٱللَّهِ وَٱشۡهَدۡ بِأَنَّا مُسۡلِمُونَ ﴾
[آل عِمران: 52]

Ndipo pamene Yesu adaona kuti iwo adalibe chikhulupiriro, iye adati: “Kodi ndani adzandithandiza ine mu ntchito ya Mulungu?” Ophunzira ake adati: Ife ndife othandiza mu ntchito ya Mulungu, Ife takhulupirira mwa Mulungu ndipo chitirani umboni kuti ife ndife Asilamu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما أحس عيسى منهم الكفر قال من أنصاري إلى الله قال الحواريون, باللغة نيانجا

﴿فلما أحس عيسى منهم الكفر قال من أنصاري إلى الله قال الحواريون﴾ [آل عِمران: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma pamene Isa (Yesu) adazindikira mwa iwo kusakhulupirira adati: “Ndani akhale athandizi anga kwa Allah (popitiriza kufalitsa Chipembedzo Chake)?” Ophunzira ake adati: “Ife ndife athandizi a Allah (pofalitsa Chipembedzo Chake). Takhulupirira Allah; ndipo ikira umboni kuti ife ndithu ndi odzipereka kwa Allah (Asilamu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek