×

Ndithudi Mulungu amawadziwa onse amene amaletsa anzawo ndi iwo amene amauza abale 33:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:18) ayat 18 in Chichewa

33:18 Surah Al-Ahzab ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 18 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿۞ قَدۡ يَعۡلَمُ ٱللَّهُ ٱلۡمُعَوِّقِينَ مِنكُمۡ وَٱلۡقَآئِلِينَ لِإِخۡوَٰنِهِمۡ هَلُمَّ إِلَيۡنَاۖ وَلَا يَأۡتُونَ ٱلۡبَأۡسَ إِلَّا قَلِيلًا ﴾
[الأحزَاب: 18]

Ndithudi Mulungu amawadziwa onse amene amaletsa anzawo ndi iwo amene amauza abale awo kuti, “Bwerani kwa ife.” Pamene iwo sadza ku nkhondo kupatula ochepa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قد يعلم الله المعوقين منكم والقائلين لإخوانهم هلم إلينا ولا يأتون البأس, باللغة نيانجا

﴿قد يعلم الله المعوقين منكم والقائلين لإخوانهم هلم إلينا ولا يأتون البأس﴾ [الأحزَاب: 18]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu Allah akuwadziwa amene akudziletsa mwa inu (kupita ku nkhondo pamodzi ndi Mtumiki (s.a.w) ndi kuletsanso anthu ena), ndi amene akuuza abale awo: “Bwerani kwa ife; (m’thaweni Muhammad {s.a.w}).” Ndiponso sapita ku nkhondo koma pang’ono pokha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek