×

Ndipo iwo adati, “oh Ambuye wathu! Titalikitsireni mitunda yoti tiziyendamo.” Ndipo iwo 34:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:19) ayat 19 in Chichewa

34:19 Surah Saba’ ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 19 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿فَقَالُواْ رَبَّنَا بَٰعِدۡ بَيۡنَ أَسۡفَارِنَا وَظَلَمُوٓاْ أَنفُسَهُمۡ فَجَعَلۡنَٰهُمۡ أَحَادِيثَ وَمَزَّقۡنَٰهُمۡ كُلَّ مُمَزَّقٍۚ إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَأٓيَٰتٖ لِّكُلِّ صَبَّارٖ شَكُورٖ ﴾
[سَبإ: 19]

Ndipo iwo adati, “oh Ambuye wathu! Titalikitsireni mitunda yoti tiziyendamo.” Ndipo iwo adzipondereza okha. Kotero Ife tidawasandutsa kukhala nkhaniimeneimakambidwakambidwandipotidawamwaza m’magulumagulu. Ndithudi mu chimenechi muli phunziro kwa aliyense amene amapirira ndi kuthokoza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فقالوا ربنا باعد بين أسفارنا وظلموا أنفسهم فجعلناهم أحاديث ومزقناهم كل ممزق, باللغة نيانجا

﴿فقالوا ربنا باعد بين أسفارنا وظلموا أنفسهم فجعلناهم أحاديث ومزقناهم كل ممزق﴾ [سَبإ: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma (adauda mtendere umenewu;) adati: “E Mbuye wathu! Talikitsani ntunda pakati pa maulendo athu; (kuyandikirana kwa midzi, sikukutisonyeza kuti tili pa ulendo).” Ndipo adadzichitira okha zoipa. Choncho tidawachita kukhala miyambi (imene anthu a pambuyo ankauzana pakati pawo), ndipo tidawabalalitsa; kubalalikana zedi. (Ena adathawira dziko ili, ena dziko lina). Ndithu m’zimenezo muli malingaliro kwa yense wopirira kwabasi ndi wothokoza kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek