×

Iwo amene ankati ndi ofoka adzati kwa iwo amene adali onyada, “Iyayi! 34:33 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:33) ayat 33 in Chichewa

34:33 Surah Saba’ ayat 33 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 33 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿وَقَالَ ٱلَّذِينَ ٱسۡتُضۡعِفُواْ لِلَّذِينَ ٱسۡتَكۡبَرُواْ بَلۡ مَكۡرُ ٱلَّيۡلِ وَٱلنَّهَارِ إِذۡ تَأۡمُرُونَنَآ أَن نَّكۡفُرَ بِٱللَّهِ وَنَجۡعَلَ لَهُۥٓ أَندَادٗاۚ وَأَسَرُّواْ ٱلنَّدَامَةَ لَمَّا رَأَوُاْ ٱلۡعَذَابَۚ وَجَعَلۡنَا ٱلۡأَغۡلَٰلَ فِيٓ أَعۡنَاقِ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْۖ هَلۡ يُجۡزَوۡنَ إِلَّا مَا كَانُواْ يَعۡمَلُونَ ﴾
[سَبإ: 33]

Iwo amene ankati ndi ofoka adzati kwa iwo amene adali onyada, “Iyayi! Inu munkakonza chiwembu usiku ndi usana ndipo mumatiuza ife kuti tisakhulupirire mwa Mulungu koma kukhazikitsa mafano kuonjezera pa Iye.” Ndipo iwo adzabisa kukhumudwa kwawo pamene adzaone chilango ndipo Ife tidzaika magoli m’makosi mwa iwo amene sadakhulupirire. Iwo sadzakhululukidwa pa zimene adachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقال الذين استضعفوا للذين استكبروا بل مكر الليل والنهار إذ تأمروننا أن, باللغة نيانجا

﴿وقال الذين استضعفوا للذين استكبروا بل مكر الليل والنهار إذ تأمروننا أن﴾ [سَبإ: 33]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene adaponderezedwa adzanena kwa amene adadzikweza: “Iyayi, koma (mumachita) ndale za usiku ndi usana (zotitsekereza nazo ku chikhulupiliro) pamene mumatilamula kuti tinkanire Allah ndikumpangira Iye milungu inzake.” Iwo adzabisa madandaulo pamene adzaona chilango. Ndipo tidzaika magoli m’makosi mwa amene sadakhulupirire; kodi angalipidwe china, osati zija ankachita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek