×

Ndipo iwo amene sakhulupirira amati, “Kodi tingakulangizeni amene amakuuzani kuti pamene inu 34:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:7) ayat 7 in Chichewa

34:7 Surah Saba’ ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 7 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿وَقَالَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ هَلۡ نَدُلُّكُمۡ عَلَىٰ رَجُلٖ يُنَبِّئُكُمۡ إِذَا مُزِّقۡتُمۡ كُلَّ مُمَزَّقٍ إِنَّكُمۡ لَفِي خَلۡقٖ جَدِيدٍ ﴾
[سَبإ: 7]

Ndipo iwo amene sakhulupirira amati, “Kodi tingakulangizeni amene amakuuzani kuti pamene inu musanduka dothi mudzalengendwanso kukhala m’badwo watsopano?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقال الذين كفروا هل ندلكم على رجل ينبئكم إذا مزقتم كل ممزق, باللغة نيانجا

﴿وقال الذين كفروا هل ندلكم على رجل ينبئكم إذا مزقتم كل ممزق﴾ [سَبإ: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo osakhulupirira akunena (pouzana pakati pawo mwachipongwe): “Kodi Tikusonyezeni za munthu yemwe akukuuzani kuti (m’kadzafa) ndi kudukaduka m’dzakhala m’kalengedwe katsopano?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek