×

Kodi inu simuona mmene Mulungu amatumizira mvula kuchokera kumwamba ndipo amaisiya kuti 39:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:21) ayat 21 in Chichewa

39:21 Surah Az-Zumar ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 21 - الزُّمَر - Page - Juz 23

﴿أَلَمۡ تَرَ أَنَّ ٱللَّهَ أَنزَلَ مِنَ ٱلسَّمَآءِ مَآءٗ فَسَلَكَهُۥ يَنَٰبِيعَ فِي ٱلۡأَرۡضِ ثُمَّ يُخۡرِجُ بِهِۦ زَرۡعٗا مُّخۡتَلِفًا أَلۡوَٰنُهُۥ ثُمَّ يَهِيجُ فَتَرَىٰهُ مُصۡفَرّٗا ثُمَّ يَجۡعَلُهُۥ حُطَٰمًاۚ إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَذِكۡرَىٰ لِأُوْلِي ٱلۡأَلۡبَٰبِ ﴾
[الزُّمَر: 21]

Kodi inu simuona mmene Mulungu amatumizira mvula kuchokera kumwamba ndipo amaisiya kuti ilowe pansi m’mitsinje? Mmene Iye amameretsera mbewu za maonekedwe osiyanasiyana zimene zimafota ndipo inu mumaziona zitasanduka zachikasu ndipo amazipanga izo kuti ziume ndi kuthetheka? Ndithudi mu zimenezi muli chikumbutso kwa anthu ozindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألم تر أن الله أنـزل من السماء ماء فسلكه ينابيع في الأرض, باللغة نيانجا

﴿ألم تر أن الله أنـزل من السماء ماء فسلكه ينابيع في الأرض﴾ [الزُّمَر: 21]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi suona kuti Allah amatsitsa madzi kuchokera kumwamba, ndipo amawalowetsa mu akasupe mkati mwa nthaka, kenako amatulutsa ndi madziwo mbewu zosiyana mitundu: (chimanga, mpunga, tirigu, ndi zina zotere). Ndipo kenako zimauma (pambuyo pokhala zobiriwira); umaziona zili zachikasu. Kenako amazichita kukhala zidutswazidutswa? Ndithu muzimenezo muli chikumbutso kwa eni nzeru (zofufuzira zinthu)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek