×

Inu simudzatha kuchita chilungamo pakati pa akazi anu ngakhale mutafuna kutero. Motero 4:129 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:129) ayat 129 in Chichewa

4:129 Surah An-Nisa’ ayat 129 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 129 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَلَن تَسۡتَطِيعُوٓاْ أَن تَعۡدِلُواْ بَيۡنَ ٱلنِّسَآءِ وَلَوۡ حَرَصۡتُمۡۖ فَلَا تَمِيلُواْ كُلَّ ٱلۡمَيۡلِ فَتَذَرُوهَا كَٱلۡمُعَلَّقَةِۚ وَإِن تُصۡلِحُواْ وَتَتَّقُواْ فَإِنَّ ٱللَّهَ كَانَ غَفُورٗا رَّحِيمٗا ﴾
[النِّسَاء: 129]

Inu simudzatha kuchita chilungamo pakati pa akazi anu ngakhale mutafuna kutero. Motero musakondere mbali imodzi ndikumusiya winayo osadziwa chimene chili kuchitika. Ndipo ngati inu muchita chilungamo ndi kuchita chili chonse chabwino ndi kuopa Mulungu, ndithudi Mulungu ndi wokhululukira ndi wachisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولن تستطيعوا أن تعدلوا بين النساء ولو حرصتم فلا تميلوا كل الميل, باللغة نيانجا

﴿ولن تستطيعوا أن تعدلوا بين النساء ولو حرصتم فلا تميلوا كل الميل﴾ [النِّسَاء: 129]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo inu simungathe kuchita chilungamo (chenicheni) pakati pa akazi ngakhale mutayesetsa chotani. Koma musapendekere (mbali imodzi); kupendekera kwathunthu kotero kuti nkumusiya (yemwe simukumfunayo) ngati kuti wapachikidwa (osadziwika kuti ngokwatiwa kapena ayi). Ndipo ngati mutayanjana ndi kuopa Allah (zingakhale bwino). Ndithudi, Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngwachisoni zedi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek