×

“Mosakayika chimene muli kundiitanira chilibe dzina m’dziko lino ndi m’dziko limene lili 40:43 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:43) ayat 43 in Chichewa

40:43 Surah Ghafir ayat 43 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 43 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿لَا جَرَمَ أَنَّمَا تَدۡعُونَنِيٓ إِلَيۡهِ لَيۡسَ لَهُۥ دَعۡوَةٞ فِي ٱلدُّنۡيَا وَلَا فِي ٱلۡأٓخِرَةِ وَأَنَّ مَرَدَّنَآ إِلَى ٱللَّهِ وَأَنَّ ٱلۡمُسۡرِفِينَ هُمۡ أَصۡحَٰبُ ٱلنَّارِ ﴾
[غَافِر: 43]

“Mosakayika chimene muli kundiitanira chilibe dzina m’dziko lino ndi m’dziko limene lili nkudza ndipo kuti tidzabwerakwa Mulungu. Ndipoonseoswamalamulo, malo awo adzakhala ku moto.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا جرم أنما تدعونني إليه ليس له دعوة في الدنيا ولا في, باللغة نيانجا

﴿لا جرم أنما تدعونني إليه ليس له دعوة في الدنيا ولا في﴾ [غَافِر: 43]

Khaled Ibrahim Betala
““Palibe chikaiko, ndithu zomwe mukundiitanirazo (kuti ndizipembedze) zilibe (kuyankha) pempho lililonse pano pa dziko lapansi ngakhale tsiku lachimaliziro. Ndipo kobwerera kwathu nkwa Allah basi. Ndipo, wopyola malire (a Allah) iwowo ndiwo anthu a ku Moto.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek