×

Ndipo Iye adakonza ndi kulenga maiko asanu ndi awiri m’masiku awiri ndipo 41:12 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Fussilat ⮕ (41:12) ayat 12 in Chichewa

41:12 Surah Fussilat ayat 12 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Fussilat ayat 12 - فُصِّلَت - Page - Juz 24

﴿فَقَضَىٰهُنَّ سَبۡعَ سَمَٰوَاتٖ فِي يَوۡمَيۡنِ وَأَوۡحَىٰ فِي كُلِّ سَمَآءٍ أَمۡرَهَاۚ وَزَيَّنَّا ٱلسَّمَآءَ ٱلدُّنۡيَا بِمَصَٰبِيحَ وَحِفۡظٗاۚ ذَٰلِكَ تَقۡدِيرُ ٱلۡعَزِيزِ ٱلۡعَلِيمِ ﴾
[فُصِّلَت: 12]

Ndipo Iye adakonza ndi kulenga maiko asanu ndi awiri m’masiku awiri ndipo adapereka ku dziko lililonse ulamuliro. Ndipo Ife tidaika ku muyamba wapansi nyenyezi zokongola kuti zizilonda. Umenewo ndi ulamuliro wa Mwini mphamvu ndi Mwini nzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فقضاهن سبع سموات في يومين وأوحى في كل سماء أمرها وزينا السماء, باللغة نيانجا

﴿فقضاهن سبع سموات في يومين وأوحى في كل سماء أمرها وزينا السماء﴾ [فُصِّلَت: 12]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho adakwaniritsa kulenga thambo zisanu ndi ziwiri mmasiku awiri, ndipo thambo lililonse adalidziwitsa ntchito yake (polilamula zochita zake). Ndipo tidakongoletsa thambo lapafupi (ndi inu) ndi nyenyezi (zounikira dziko lapansi), ndiponso kuti zizilondera kumwamha (kuti ziwanda zisamapite kukamvera za kumwamba). Uwu ndi muyeso wa Mwini mphamvu, Wodziwa kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek