×

Nena, “Ndiuzeni ngati ilo ndi lochokera kwa Mulungu ndipo inu muli kulikana. 41:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Fussilat ⮕ (41:52) ayat 52 in Chichewa

41:52 Surah Fussilat ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Fussilat ayat 52 - فُصِّلَت - Page - Juz 25

﴿قُلۡ أَرَءَيۡتُمۡ إِن كَانَ مِنۡ عِندِ ٱللَّهِ ثُمَّ كَفَرۡتُم بِهِۦ مَنۡ أَضَلُّ مِمَّنۡ هُوَ فِي شِقَاقِۭ بَعِيدٖ ﴾
[فُصِّلَت: 52]

Nena, “Ndiuzeni ngati ilo ndi lochokera kwa Mulungu ndipo inu muli kulikana. Kodi ndani amene angakhale wolakwa kwambiri kuposa iye amene amatsutsa mowirikiza?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل أرأيتم إن كان من عند الله ثم كفرتم به من أضل, باللغة نيانجا

﴿قل أرأيتم إن كان من عند الله ثم كفرتم به من أضل﴾ [فُصِّلَت: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena (kwa iwo, iwe Mtumiki): “Tandiuzani ngati (Qur’aniyi) ilidi yochokera kwa Allah, kenako inu nkuikanira; (nanga zingakhale bwanji?) Kodi ndiyani wosokera kwambiri kuposa uyo amene ali mu mtsutso wakutali (ndi choona)?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek