Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zukhruf ayat 87 - الزُّخرُف - Page - Juz 25
﴿وَلَئِن سَأَلۡتَهُم مَّنۡ خَلَقَهُمۡ لَيَقُولُنَّ ٱللَّهُۖ فَأَنَّىٰ يُؤۡفَكُونَ ﴾
[الزُّخرُف: 87]
﴿ولئن سألتهم من خلقهم ليقولن الله فأنى يؤفكون﴾ [الزُّخرُف: 87]
Khaled Ibrahim Betala “Ndipo ngati utawafunsa: “Ndani adawalenga?” Anena motsimikiza kuti: “Ndi Allah.” Nanga akutembenuzidwa bwanji (kusiya choona) |